Levitiko 22:13 BL92

13 Koma mwana wamkazi wa wansembe akakhala wamasiye kapena wocotsedwa, ndipo alibe mwana, nabwerera ku nyumba ya atate wace, monga muja anali mwana, adyeko mkate wa atate wace; koma mlendo asamadyako.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 22

Onani Levitiko 22:13 nkhani