Levitiko 22:3 BL92

3 Nena nao, Ali yense wa mbeu zanu zonse mwa mibadwo yanu, akayandikiza zinthu zopatulika, zimene ana a Israyeli azipatulira Yehova, pokhala ali naco comdetsa cace, azimsadza munthuyo pankhope panga; Ine ndine Yehova.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 22

Onani Levitiko 22:3 nkhani