Levitiko 22:4 BL92

4 Munthu ali yense wa mbeu za Aroni wokhala ndi khate, kapena kukha, asadyeko zinthu zopatulika, kufikira atayera. Ndipo ali yense wokhudza cinthu codetsedwa ndi wakufa, kapena mwamuna wogona uipa;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 22

Onani Levitiko 22:4 nkhani