Levitiko 5:1 BL92

1 Ndipo akacimwa munthu, wakuti adamva mau akuwalumbiritsa, ndiye mboni, kapena wakuona, kapena wakudziwa, koma osaulula, azisenza mphulupulu yace;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 5

Onani Levitiko 5:1 nkhani