Levitiko 5:12 BL92

12 Ndipo adze naco kwa wansembe, ndi wansembeyo atengeko wodzala manja ukhale cikumbutso cace, nacitenthe pa guwa la nsembe monga umo amacitira nsembe zamoto za Yehova; ndiyo nsembe yaucimo.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 5

Onani Levitiko 5:12 nkhani