Levitiko 5:13 BL92

13 Ndipo wansembe amcitire comtetezera cifukwa ca kucimwa kwace adacimwira cimodzi ca izi, ndipo adzakhululukidwa; ndipo cotsalira cikhale ca wansembe, monga umo amacitira copereka caufaco.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 5

Onani Levitiko 5:13 nkhani