24 Ndipo unaturuka mota pamaso ya Yehova, nunyeketsa nsembe yopsereza ndi mafuta pa guwa la nsembe; ndipo pakuciona anthu onse anapfuula, nagwa nkhope zao pansi.
Werengani mutu wathunthu Levitiko 9
Onani Levitiko 9:24 nkhani