1 Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yace ya zofukiza, naikamo moto, naikapo cofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wacilendo, umene sanawauza.
Werengani mutu wathunthu Levitiko 10
Onani Levitiko 10:1 nkhani