Levitiko 26:44 BL92

44 Ndiponso pali icinso: pokhala iwo m'dziko la adani ao sindidzawakaniza, kapena kunyansidwa nao, kuwaononga konse, ndi kutyola pangano langa ndinapangana nao; popeza Ine ndine Yehova Muhmgu wao.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 26

Onani Levitiko 26:44 nkhani