Mateyu 12:11 BL92

11 Koma Iye anati kwa iwo, Munthu ndani wa inu, amene ali nayo nkhosa imodzi, ndipo ngati idzagwa m'dzenje tsiku la Sabata, kodi sadzaigwira, ndi kuiturutsa?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 12

Onani Mateyu 12:11 nkhani