Mateyu 12:29 BL92

29 Kapena akhoza bwanji munthu kulowa m'banja la munthu wolimba, ndi kufunkha akatundu ace, ngati iye sayamba kumanga munthu wolimbayo? ndipo pamenepo adzafunkha za m'banja lace.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 12

Onani Mateyu 12:29 nkhani