Mateyu 13:52 BL92

52 Ndipo Iye anati kwa iwo, Cifukwa cace, mlembi ali yense, wophunzitsidwa mu Ufumu wa Kumwamba, ali wofanana ndi munthu mwini banja, amene aturutsa m'cuma cace zinthu zakale ndi zatsopano.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 13

Onani Mateyu 13:52 nkhani