Mateyu 16:27 BL92

27 Pakuti Mwana wa munthu adzabwera mu ulemerero wa Atate wace, pamodzi ndi angelo ace; ndipo pomwepo Iye adzabwezera kwa anthu onse monga macitidwe ao.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 16

Onani Mateyu 16:27 nkhani