Mateyu 17:9 BL92

9 Ndipo pamene anali kutsika paphiri, Yesu anawalangiza iwo kuti, Musakauze munthu coonekaco, kufikira Mwana wa munthu adadzauka kwa akufa.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 17

Onani Mateyu 17:9 nkhani