Mateyu 18:12 BL92

12 Nanga muyesa bwanji? ngati munthu ali nazo nkhosa makumi khumi, ndipo ikasokera imodzi ya izo, kodi saleka zija makumi asanu ndi anai mphambu manu ndi zinai, napita kumapiri, kukafuna yosokerayo?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 18

Onani Mateyu 18:12 nkhani