Mateyu 18:16 BL92

16 Koma ngati samvera, onjeza kutenga ndi iwe wina mmodzi kapena awiri, kuti atsimikizidwe mau onse pakamwa pa mboni ziwiri kapena zitatu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 18

Onani Mateyu 18:16 nkhani