Mateyu 18:6 BL92

6 koma yense amene adzakhumudwitsa kamodzi ka tiana iti, takukhulupirira Ine, kumuyenera iye kuti mphero yaikuru ikolowekedwe m'khosi mwace, namizidwe poya pa nyanja.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 18

Onani Mateyu 18:6 nkhani