Mateyu 19:23 BL92

23 Ndipo Yesu anati kwa ophunzira ace, Indetu ndinena kwa inu, kuti munthu mwini cuma adzalowa mobvutika mu Ufumu wa Kumwamba.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 19

Onani Mateyu 19:23 nkhani