Mateyu 19:27 BL92

27 Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, Onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi ciani?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 19

Onani Mateyu 19:27 nkhani