Mateyu 19:29 BL92

29 Ndipo onse amene adasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena atate, kapena amai, kapena ana, kapena minda, cifukwa ca dzina langa, adzalandira zobwezeredwa zambirimbiri, nadzalowa moyo wosatha.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 19

Onani Mateyu 19:29 nkhani