Mateyu 2:9 BL92

9 Ndipo iwo, m'mene anamva mfumu, anamuka; ndipo onani, nyenyezi ija anaiona kum'mawa, inawatsogolera iwo, kufikira inadza niima pamwamba pomwe panali kamwanako.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 2

Onani Mateyu 2:9 nkhani