Mateyu 20:23 BL92

23 Iye ananena kwa iwo, Cikho canga mudzamweradi; koma kukhala ku dzanja lamanja kwangandi kulamanzere, sikuli kwanga kupatsa, koma kuli kwa iwo omwe kwakonzedweratu ndi Atate wanga.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 20

Onani Mateyu 20:23 nkhani