Mateyu 21:25 BL92

25 Ubatizo wa Yohane, ucokera kuti? Kumwamba kodi kapena kwa anthu? Koma iwo anafunsana wina ndi mnzace, kuti, Tikati, Kumwamba, Iye adzati kwa ife, Munalekeranji kumvera iye?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 21

Onani Mateyu 21:25 nkhani