Mateyu 21:41 BL92

41 Iwo ananena kwa Iye, Adzaononga koipa oipawo, nadzapereka mundawo kwa olima ena, amene adzambwezera iye zipatso pa nyengo zace.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 21

Onani Mateyu 21:41 nkhani