Mateyu 21:9 BL92

9 Ndipo mipingo yakumtsogolera ndi yakumtsatira, inapfuula, kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide! Wolemekezeka ndiye wakudza m'dzina la Ambuye! Hosana m'Kumwambamwamba!

Werengani mutu wathunthu Mateyu 21

Onani Mateyu 21:9 nkhani