Mateyu 22:21 BL92

21 Nanena iwo, Ca Kaisara. Pomwepo Iye anati kwa iwo, Cifukwa cace patsani kwa Kaisara zace za Kaisara, ndi kwa Mulungu zace za Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 22

Onani Mateyu 22:21 nkhani