Mateyu 23:27 BL92

27 Tsoka inu, alembi ndi Afarisi, onyenga! cifukwa mufanafana ndi manda opaka njereza, amene aonekera okoma kunja kwace, koma adzala m'katimo ndi mafupa a anthu akufa ndi zonyansa zonse.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 23

Onani Mateyu 23:27 nkhani