Mateyu 24:24 BL92

24 cifukwa Akristu onama adzauka, ndi aneneri onama nadzaonetsa zizindikiro zazikuru ndi zozizwa: kotero kuti akanyenge, ngati nkotheka, osankhidwa omwe. Onani ndakuuziranitu pasadafike.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 24

Onani Mateyu 24:24 nkhani