Mateyu 25:20 BL92

20 Ndipo uyo amene adalandira ndalama za matalente zisanu anadza, ali nazo ndalama zina zisanu, nanena, Mbuye, munandipatsa ndalama za matalente, zisanu, onani ndapindulapo ndalama zisanu zina.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 25

Onani Mateyu 25:20 nkhani