Mateyu 25:26 BL92

26 Koma mbuye wace anayankha, nati kwa iye, Kapolo iwe woipa ndi waulesi, unadziwa kuti ndimatuta kumene sindinafesa, ndi kusonkhanitsa kumene sindinawaza;

Werengani mutu wathunthu Mateyu 25

Onani Mateyu 25:26 nkhani