Mateyu 25:41 BL92

41 Pomwepo Iye adzanena kwa iwo a ku dzanja lamanzere, Cokani kwa Ine otembereredwa inu, ku mota wa nthawi zonse wokolezedwera mdierekezi ndi amithenga ace:

Werengani mutu wathunthu Mateyu 25

Onani Mateyu 25:41 nkhani