Mateyu 26:18 BL92

18 Nati Iye, Mukani kumzinda kwa munthu wangana, mukati kwa iye, Mphunzitsi anena. Nthawi yanga yayandikirai ndidzadya Paskha kwanu pamodzi ndi ophunzira anga.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 26

Onani Mateyu 26:18 nkhani