Mateyu 26:63 BL92

63 Koma 4 Yesu anangokhala cete. Ndipo mkuru wa ansembe ananena kwa Iye, Ndikulumbiritsa Iwe pa Mulungu wamoyo, kuti utiuze ife ngati Iwe ndiwe Kristu, Mwana wa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 26

Onani Mateyu 26:63 nkhani