Mateyu 26:65 BL92

65 Pomwepo mkuru wa ansembe 6 anang'amba zobvala zace, nati, Acitira Mulungu mwano; tifuniranji mboni zina? onani, tsopano mwamva mwanowo;

Werengani mutu wathunthu Mateyu 26

Onani Mateyu 26:65 nkhani