Mateyu 26:75 BL92

75 Ndipo Petro anakumbukira mau amene Yesu adati, 12 Asanalire tambala udzandikana katatu. Ndipo anaturukira kunja, nalira ndi kuwawa mtima.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 26

Onani Mateyu 26:75 nkhani