Mateyu 27:29 BL92

29 Ndipo analuka korona waminga, nambveka pamutu pace, namgwiritsa bango m'dzanja lamanja lace; ndipo anagwada pansi pamaso pace, namcitira cipongwe, nati, Tikuoneni, Mfumu ya Ayuda!

Werengani mutu wathunthu Mateyu 27

Onani Mateyu 27:29 nkhani