Mateyu 27:46 BL92

46 Ndipo poyandikira ora lacisanu ndi cinai, Yesu 7 anapfuula ndi mau akuru, kunena, Eli, Eli, lama sabakitani? ndiko kunena kuti, Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 27

Onani Mateyu 27:46 nkhani