Mateyu 27:64 BL92

64 Cifukwa cace mulamule kuti asindikize pamandapo, kufikira tsiku lacitatulo, kuti kapena ophunzira ace angadze, nadzamuba Iye, nadzanena kwa anthu, kuti Iye anauka kwa akufa: ndipo cinyengo comariza cidzaposa coyambaco.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 27

Onani Mateyu 27:64 nkhani