Mateyu 3:7 BL92

7 Ndipo iye pakuona ambiri a Afarisi ndi a Asaduki akudza ku ubatizo wace, anati kwa iwo, Obadwa a njoka inu, ndani anakulangizani kuthawa mkwiyo ulinkudza?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 3

Onani Mateyu 3:7 nkhani