Mateyu 3:9 BL92

9 ndipo musamayesa kunena mwa inu nokha, Atate wathu tiri naye Abrahamu; pakuti ndinena kwa inu kuti mwa miyala iyi Mulungu akhoza kuukitsira Abrahamu ana.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 3

Onani Mateyu 3:9 nkhani