Mateyu 4:18 BL92

18 Ndipo pamene Yesu analikuyenda m'mbali mwa nyanja ya Galileya, anaona abale awiri, Simoni wonenedwa Petro, ndi Andreya, mbale wace, analikuponya psasa m'nyanja; popeza anali asodzi a nsomba.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 4

Onani Mateyu 4:18 nkhani