Mateyu 4:23 BL92

23 Ndipo Yesu anayendayenda m'Galileya monse, analikuphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira uthenga wabwino wa Ufumu, naciritsa nthenda zonse ndi kudwala konse mwa anthu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 4

Onani Mateyu 4:23 nkhani