Mateyu 5:32 BL92

32 koma Ine ndinena kwa inu, kuti 4 yense wakucotsa mkazi wace, kosati cifukwa ca cigololo, amcititsa cigololo: ndipo amene adzakwata wocotsedwayo acita cigololo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 5

Onani Mateyu 5:32 nkhani