Mateyu 6:1 BL92

1 Yang'anirani kuti musacite zolungama zanu pamaso pa anthu kuti muonekere kwa iwo; pakuti ngati mutero mulibe mphotho ndi Atate wanu wa Kumwamba.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:1 nkhani