Mateyu 6:5 BL92

5 Ndipo pamene mupemphera, musakhale monga onyengawo; cifukwa iwo akonda kuimirira ndi kupemphera m'masunagoge, ndi pa mphambano za makwalala, kuti aonekere kwa anthu. Indetu ndinena kwa inu, Iwo alandiriratu mphotho zao.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:5 nkhani