Mateyu 6:7 BL92

7 Ndipo popemphera musabwereze-bwereze cabe iai, monga amacita anthu akunja, cifukwa ayesa kuti adzamvedwa ndi kulankhula-lankhula kwao.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:7 nkhani