Mateyu 7:11 BL92

11 Comweco, ngati inu, muli oipa, mudziwa kupatsa ana anu mphatso zabwino, kopambana kotani nanga Atate wanu wa Kumwamba adzapatsa zinthu zabwino kwa iwo akumpempha Iye?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 7

Onani Mateyu 7:11 nkhani