Mateyu 8:20 BL92

20 Ndipo Yesu ananena kwa iye, Ankhandwe ali nazo nkhwimba zao, ndi mbalame za m'mlengalenga zisa zao, koma Mwana wa munthu alibe potsamira mutu wace.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 8

Onani Mateyu 8:20 nkhani