Mateyu 9:22 BL92

22 Koma Yesu potembenuka ndi kuona iye anati, Limba mtima, mwana wamkaziwe, cikhulupiriro cako cakuciritsa. Ndipo mkaziyo anacira kuyambira nthawi yomweyo.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 9

Onani Mateyu 9:22 nkhani