Mateyu 9:27 BL92

27 Ndipo popita Yesu kucokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, opfuula ndi kuti, Muticitire ife cifundo, mwana wa Davide.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 9

Onani Mateyu 9:27 nkhani